Logo YouVersion
Icona Cerca

Gen. 3:16

Gen. 3:16 BLY-DC

Pambuyo pake Mulungu adauza mkaziyo kuti, “Ndidzaonjeza zovuta zako pamene udzakhala ndi pathupi, udzamva zoŵaŵa pa nthaŵi yako ya kubala mwana. Udzakhumba mwamuna wako, ndipo mwamuna wakoyo adzakulamulira iwe.”

Leggi Gen. 3

Video per Gen. 3:16