Genesis 1:29

Genesis 1:29 CCL

Kenaka Mulungu anati, “Ine ndakupatsani chomera chilichonse cha pa dziko lapansi chimene chili ndi mbewu komanso mtengo uliwonse wobala zipatso zokhala ndi mbewu mʼkati mwake kuti zikhale chakudya chanu.

Rencana Bacaan dan Renungan gratis terkait dengan Genesis 1:29