Logo YouVersion
AlkitabRencanaVideo
Dapatkan Aplikasinya
Pemilih Bahasa
Ikon Pencarian

Ayat-ayat Alkitab Ternama dari Genesis 2

1

Genesis 2:24

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nʼchifukwa chake, mwamuna amasiya abambo ndi amayi ake nakaphatikana ndi mkazi wake ndipo awiriwo amakhala thupi limodzi.

Bandingkan

Telusuri Genesis 2:24

2

Genesis 2:18

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Yehova Mulungu anati, “Sibwino kuti munthu akhale yekha. Ndidzamupangira mnzake womuthandiza.”

Bandingkan

Telusuri Genesis 2:18

3

Genesis 2:7

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono Yehova Mulungu anawumba munthu kuchokera ku dothi nawuziramo mpweya wamoyo mʼmphuno mwake ndipo munthuyo anakhala wamoyo.

Bandingkan

Telusuri Genesis 2:7

4

Genesis 2:23

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Munthu uja anati, “Uyu ndiye fupa lochokera ku mafupa anga ndi mnofu wochokera ku mnofu wanga; adzatchedwa ‘mkazi,’ popeza wachokera mwa mwamuna.”

Bandingkan

Telusuri Genesis 2:23

5

Genesis 2:3

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Mulungu anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri nalipatula, chifukwa pa tsiku limeneli Iye anapumula ku ntchito yonse yolenga imene anayigwira.

Bandingkan

Telusuri Genesis 2:3

6

Genesis 2:25

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Munthu uja ndi mkazi wakeyo, onse awiri anali maliseche ndipo analibe manyazi.

Bandingkan

Telusuri Genesis 2:25

Rencana Bacaan dan Renungan gratis terkait dengan Genesis 2

Pasal Sebelumnya
Pasal Berikutnya
YouVersion

Mendorong dan menantang Anda mencari keintiman dengan Tuhan setiap hari.

Pelayanan

Tentang

Karier

Sukarelawan

Blog

Pers

Tautan Berguna

Bantuan

Sumbang

Versi Alkitab

Alkitab Audio

Bahasa Alkitab

Ayat Hari Ini


Pelayanan Digital dari

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Kebijakan PrivasiSyarat
Program Pengungkapan Kerentanan
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Beranda

Alkitab

Rencana

Video