YouVersion logo
Ikona pretraživanja

YOHANE 13:4-5

YOHANE 13:4-5 BLP-2018

ananyamuka pamgonero, navula malaya ake; ndipo m'mene adatenga chopukutira, anadzimanga m'chuuno. Pomwepo anathira madzi m'beseni, nayamba kusambitsa mapazi a ophunzira ake, ndi kuwapukuta ndi chopukutira, chimene anadzimanga nacho.

Videozapis za YOHANE 13:4-5