1
GENESIS 19:26
Buku Lopatulika
Koma mkazi wake anacheuka ali pambuyo pake pa Loti, nasanduka mwala wamchere.
Usporedi
Istraži GENESIS 19:26
2
GENESIS 19:16
Koma anachedwa; ndipo anthuwo anamgwira dzanja lake, ndi dzanja la mkazi wake ndi dzanja la ana ake aakazi awiri; chifukwa cha kumchitira chifundo Yehova; ndipo anamtulutsa iye, namuika kunja kwa mzinda.
Istraži GENESIS 19:16
3
GENESIS 19:17
Ndipo panali pamene anawatulutsa iwo kunja, anati, Tapulumuka ndi moyo wako; usacheuke, usakhale pachigwa paliponse; thawira kuphiri, kuti unganyeke.
Istraži GENESIS 19:17
4
GENESIS 19:29
Ndipo panali pamene Mulungu anaononga mizinda ya m'chigwa, Mulungu anakumbukira Abrahamu, natulutsa Loti pakati pa chionongeko, pamene anaononga mizinda m'mene anakhalamo Loti.
Istraži GENESIS 19:29
Početna
Biblija
Planovi
Videozapisi