1
Lk. 22:42
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Adati, “Atate, ngati mukufuna, mundichotsere chikho chamasautsochi. Komabe muchite zimene mukufuna Inu, osati zimene ndikufuna Ine ai.”
Compare
Lk. 22:42 ખોજ કરો
2
Lk. 22:32
Koma Ine ndakupempherera, kuti usaleke kundikhulupirira. Ndipo iweyo utatembenuka mtima, ukaŵalimbitse abale akoŵa.”
Lk. 22:32 ખોજ કરો
3
Lk. 22:19
Kenaka Yesu adatenga mkate, nathokoza Mulungu, nkuunyemanyema, nagawira ophunzira aja, ndipo adati, “Ili ndi thupi langa limene likuperekedwa chifukwa cha inu. Muzichita zimenezi kuti muzindikumbukira.”
Lk. 22:19 ખોજ કરો
4
Lk. 22:20
Atatha kudya, adaŵapatsanso chikho, nati, “Chikhochi ndi chipangano chatsopano chimene magazi anga, omwe akukhetsedwa chifukwa cha inu, akuchitsimikizira.
Lk. 22:20 ખોજ કરો
5
Lk. 22:44
Koma Yesu adavutikabe koopsa mu mtima, nkumapemphera kolimba kuposa kale. Ndipo thukuta limene ankadza linali ngati madontho akuluakulu a magazi ogwera pansi.]
Lk. 22:44 ખોજ કરો
6
Lk. 22:26
Koma pakati pa inu zisamatero ai. Kwenikweni wamkulu mwa inu azikhala ngati wamng'ono mwa onse, ndipo mtsogoleri azikhala ngati wotumikira.
Lk. 22:26 ખોજ કરો
7
Lk. 22:34
Koma Yesu adamuyankha kuti, “Ndikukuuza, iwe Petro, kuti lero lomwe lino, tambala asanalire, ukhala utandikana katatu kuti Ine sundidziŵa.”
Lk. 22:34 ખોજ કરો
હોમ
બાઇબલ
યોજનાઓ
વિડિઓઝ