YouVersion Logo
બાઇબલયોજનાઓવિડિઓઝ
Get the app
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from GENESIS 7

1

GENESIS 7:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.

Compare

GENESIS 7:1 ખોજ કરો

2

GENESIS 7:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Compare

GENESIS 7:24 ખોજ કરો

3

GENESIS 7:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.

Compare

GENESIS 7:11 ખોજ કરો

4

GENESIS 7:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali pa dziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa pa dziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.

Compare

GENESIS 7:23 ખોજ કરો

5

GENESIS 7:12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo mvula inali pa dziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.

Compare

GENESIS 7:12 ખોજ કરો

મફત વાંચન યોજનાઓ અને GENESIS 7થી સંબંધિત મનન

Previous Chapter
Next Chapter
YouVersion

Encouraging and challenging you to seek intimacy with God every day.

Ministry

વિષે

Careers

સ્વયંસેવક

બ્લોગ

દબાવો

Useful Links

સહાય કરો

દાન કરો

બાઇબલ આવૃત્તિઓ

ઑડિયો બાઇબલ

Bible Languages

આજનું વચન


A Digital Ministry of

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

ગોપનીયતા નીતિશરતો
Vulnerability Disclosure Program
ફેસબુકટ્વીટરઇન્સ્ટાગ્રામYouTubePinterest

હોમ

બાઇબલ

યોજનાઓ

વિડિઓઝ