1
GENESIS 45:5
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Tsopano musapwetekwe mtima, musadzikwiyira inu nokha, kuti munandigulitsa ine kuno, pakuti Mulungu ananditumiza ine patsogolo panu kuti ndisunge moyo.
Compare
GENESIS 45:5 ખોજ કરો
2
GENESIS 45:8
Ndipo tsopano sindinu amene munanditumiza ine ndifike kuno, koma Mulungu, ndipo anandiyesa ine atate wa Farao, ndi mwini banja lake lonse, ndi wolamulira dziko lonse la Ejipito.
GENESIS 45:8 ખોજ કરો
3
GENESIS 45:7
Ndipo Mulungu anatumiza ine patsogolo panu kuti ndikhazike inu mutsale m'dziko lapansi, ndi kusunga inu amoyo ndi chipulumutso chachikulu.
GENESIS 45:7 ખોજ કરો
4
GENESIS 45:4
Ndipo Yosefe anati kwa abale ake, Muyandikiretu kwa ine; nayandikira. Ndipo iye anati, Ine ndine Yosefe mbale wanu, ine ndemwe munandigulitsa ndilowe m'Ejipito.
GENESIS 45:4 ખોજ કરો
5
GENESIS 45:6
Zaka ziwirizi muli njala m'dziko muno; ndipo zatsala zaka zisanu, zopanda kulima kapena kusenga.
GENESIS 45:6 ખોજ કરો
6
GENESIS 45:3
Ndipo Yosefe anati kwa abale ake, Ine ndine Yosefe; kodi akali ndi moyo atate wanga? Ndipo abale ake sanakhoze kumyankha iye; pakuti anavutidwa pakumuona iye.
GENESIS 45:3 ખોજ કરો
હોમ
બાઇબલ
યોજનાઓ
વિડિઓઝ