1
Genesis 2:24
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Nʼchifukwa chake, mwamuna amasiya abambo ndi amayi ake nakaphatikana ndi mkazi wake ndipo awiriwo amakhala thupi limodzi.
مقایسه
Genesis 2:24 را جستجو کنید
2
Genesis 2:18
Ndipo Yehova Mulungu anati, “Sibwino kuti munthu akhale yekha. Ndidzamupangira mnzake womuthandiza.”
Genesis 2:18 را جستجو کنید
3
Genesis 2:7
Tsono Yehova Mulungu anawumba munthu kuchokera ku dothi nawuziramo mpweya wamoyo mʼmphuno mwake ndipo munthuyo anakhala wamoyo.
Genesis 2:7 را جستجو کنید
4
Genesis 2:23
Munthu uja anati, “Uyu ndiye fupa lochokera ku mafupa anga ndi mnofu wochokera ku mnofu wanga; adzatchedwa ‘mkazi,’ popeza wachokera mwa mwamuna.”
Genesis 2:23 را جستجو کنید
5
Genesis 2:3
Ndipo Mulungu anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri nalipatula, chifukwa pa tsiku limeneli Iye anapumula ku ntchito yonse yolenga imene anayigwira.
Genesis 2:3 را جستجو کنید
6
Genesis 2:25
Munthu uja ndi mkazi wakeyo, onse awiri anali maliseche ndipo analibe manyazi.
Genesis 2:25 را جستجو کنید
YouVersion از کوکی ها برای شخصی سازی تجربه شما استفاده می کند. با استفاده از وب سایت ما، استفاده ما از کوکی ها را همانطور که در خط مشی رازداریتوضیح داده شده است، می پذیرید
خانه
كتابمقدس
برنامههای مطالعه
ویدیوها