1
LUKA 12:40
Buku Lopatulika
Khalani okonzeka inunso; chifukwa nthawi imene simulingirira, Mwana wa Munthu akudza.
مقایسه
LUKA 12:40 را جستجو کنید
2
LUKA 12:31
Komatu tafunafunani Ufumu wake, ndipo izi adzakuonjezerani.
LUKA 12:31 را جستجو کنید
3
LUKA 12:15
Ndipo Iye anati kwa iwo, Yang'anirani, mudzisungire kupewa msiriro uliwonse; chifukwa moyo wake wa munthu sulingana ndi kuchuluka kwa zinthu zake ali nazo.
LUKA 12:15 را جستجو کنید
4
LUKA 12:34
Pakuti kumene kuli chuma chanu, komweko kudzakhalanso mtima wanu.
LUKA 12:34 را جستجو کنید
5
LUKA 12:25
Ndipo ndani wa inu, ndi kuda nkhawa angathe kuonjeza mkono pa msinkhu wake?
LUKA 12:25 را جستجو کنید
6
LUKA 12:22
Ndipo Iye anati kwa ophunzira ake, Chifukwa chake ndinena ndinu, Musade nkhawa ndi moyo wanu, chimene mudzadya; kapena ndi thupi lanu, chimene mudzavala.
LUKA 12:22 را جستجو کنید
7
LUKA 12:7
komatu ngakhale matsitsi onse a pamutu panu awerengedwa. Musaopa, muposa mtengo wake wa mpheta zambiri.
LUKA 12:7 را جستجو کنید
8
LUKA 12:32
Musaopa, kagulu ka nkhosa inu; chifukwa Atate wanu akonda kukupatsani Ufumu.
LUKA 12:32 را جستجو کنید
9
LUKA 12:24
Lingirirani makwangwala, kuti samafesai, kapena kutemai; alibe nyumba yosungiramo, kapena nkhokwe; ndipo Mulungu awadyetsa; nanga inu simuziposa mbalame kwambiri!
LUKA 12:24 را جستجو کنید
10
LUKA 12:29
Ndipo inu musafunefune chimene mudzadya, ndi chimene mudzamwa; ndipo musakayike mtima.
LUKA 12:29 را جستجو کنید
11
LUKA 12:28
Koma ngati Mulungu aveka kotere udzu wakuthengo ukhala lero, ndipo mawa uponyedwa pamoto; nanga inu sadzakuninkhani koposa, inu okhulupirira pang'ono?
LUKA 12:28 را جستجو کنید
12
LUKA 12:2
Koma kulibe kanthu kovundikiridwa kamene sikadzaululidwa; ndi kobisika kamene sikadzadziwika.
LUKA 12:2 را جستجو کنید
خانه
كتابمقدس
برنامههای مطالعه
ویدیوها