1
YOHANE 11:25-26
Buku Lopatulika
Yesu anati kwa iye, Ine ndine kuuka ndi moyo: wokhulupirira Ine, angakhale amwalira, adzakhala ndi moyo; ndipo yense wakukhala ndi moyo, nakhulupirira Ine, sadzamwalira nthawi yonse. Kodi ukhulupirira ichi?
مقایسه
YOHANE 11:25-26 را جستجو کنید
2
YOHANE 11:40
Yesu ananena naye, Kodi sindinati kwa iwe, kuti, ngati ukhulupirira, udzaona ulemerero wa Mulungu?
YOHANE 11:40 را جستجو کنید
3
YOHANE 11:35
Yesu analira.
YOHANE 11:35 را جستجو کنید
4
YOHANE 11:4
Koma Yesu pamene anamva, anati, Kudwala kumene sikuli kwa imfa, koma chifukwa cha ulemerero wa Mulungu, kuti Mwana wa Mulungu alemekezedwe nako.
YOHANE 11:4 را جستجو کنید
5
YOHANE 11:43-44
Ndipo m'mene adanena izi, anafuula ndi mau aakulu, Lazaro, tuluka. Ndipo womwalirayo anatuluka womangidwa miyendo ndi manja ndi nsalu za kumanda; ndi nkhope yake inazingidwa ndi mlezo. Yesu ananena nao, Mmasuleni iye, ndipo mlekeni amuke.
YOHANE 11:43-44 را جستجو کنید
6
YOHANE 11:38
Pamenepo Yesu, ndi kudzumanso mwa Iye yekha anadza kumanda. Koma panali phanga, ndipo mwala unaikidwa pamenepo.
YOHANE 11:38 را جستجو کنید
7
YOHANE 11:11
Izi anati, ndipo zitatha izi ananena nao, Lazaro bwenzi lathu ali m'tulo; koma ndimuka kukamuukitsa iye tulo take.
YOHANE 11:11 را جستجو کنید
خانه
كتابمقدس
برنامههای مطالعه
ویدیوها