1
Genesis 10:8
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Kusi anabereka Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
Compara
Explorar Genesis 10:8
2
Genesis 10:9
Iye anali mlenje wamphamvu kwambiri pamaso pa Yehova; nʼchifukwa chake anthu ali ndi chisudzo, chakuti, “Ndiwe mlenje wamphamvu kwambiri pamaso pa Yehova monga Nimurodi.”
Explorar Genesis 10:9
Inici
La Bíblia
Plans
Vídeos