HAGAI Mau Oyamba
Mau Oyamba
Mneneriyu adalalika mau ake chaka cha 520 BC., Ayuda ena atabwerera ku Yerusalemu kuchokera ku ukapolo. Anthuwo anali atabwerera ku ukapolo namakhala ku Yerusalemu kwa zaka zingapo, koma Kachisi anali bwinja lenileni. Atsogoleri anapereka uthenga kwa anthu kuti amangenso Kachisi, ndipo Ambuye akulonjeza kuti m'tsogolo anthu ake adzakhala pabwino ndi pa mtendere.
Za mkatimu
Yehova awalamula kuti amangenso Nyumba yake 1.1-15
Mau ena owalimbitsa mtima Ayudawo 2.1-23
Currently Selected:
HAGAI Mau Oyamba: BLPB2014
Highlight
Share
Copy

Want to have your highlights saved across all your devices? Sign up or sign in
The Bible in Chichewa Published as Buku Lopatulika
Bible Society of Malawi