YouVersion Logo
Search Icon

AMOSI 7:14-15

AMOSI 7:14-15 BLPB2014

Pamenepo Amosi anayankha, nati kwa Amaziya, Sindinali mneneri, kapena mwana wa mneneri, koma ndinali woweta ng'ombe, ndi wakutchera nkhuyu; ndipo Yehova ananditenga ndilikutsata nkhosa, nati kwa ine Yehova, Muka, nenera kwa anthu anga Israele.

Free Reading Plans and Devotionals related to AMOSI 7:14-15