YouVersion Logo
Search Icon

1 PETRO 1:6-7

1 PETRO 1:6-7 BLPB2014

M'menemo mukondwera, kungakhale tsopano kanthawi, ngati kuyenera, mukachitidwe chisoni ndi mayesero a mitundumitundu, kuti mayesedwe a chikhulupiriro chanu, ndiwo a mtengo wake woposa wa golide amene angotayika, ngakhale ayesedwa ndi moto, akapezedwe ochitira chiyamiko ndi ulemerero ndi ulemu pa vumbulutso la Yesu Khristu

Free Reading Plans and Devotionals related to 1 PETRO 1:6-7