1
Gen. 38:10
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Tsono zimene ankachitazo zidaipira Chauta ndipo Chauta adamlanganso ndi imfa.
Compare
Explore Gen. 38:10
2
Gen. 38:9
Koma Onani adaadziŵa kuti anawo sadzakhala ake. Motero nthaŵi zonse akamakhala naye mkaziyo, ankangotayira pansi mbeu yake, kuti asamubalire ana mbale wakeyo.
Explore Gen. 38:9
Home
Bible
Plans
Videos