1
Gen. 25:23
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Chauta adamuuza kuti, “M'mimba mwako muli mitundu iŵiri ya anthu. Udzabereka mafuko a anthu olimbana: mwana wina adzakhala wamphamvu kupambana mnzake, wamkulu adzakhala wotumikira wamng'ono.”
Compare
Explore Gen. 25:23
2
Gen. 25:30
Anali ndi njala zedi, motero adauza Yakobe kuti, “Ine njala yandipha. Patseko nyemba zofiira waphikazi.” (Nchifukwa chake adamutcha Edomu.)
Explore Gen. 25:30
3
Gen. 25:21
Tsono poti mkazi wa Isaki anali wosabereka, Isakiyo adapempherera mkazi wake kwa Chauta. Chauta adamva pemphero lake, ndipo Rebeka adatenga pathupi.
Explore Gen. 25:21
4
Gen. 25:32-33
Esau adati, “Chabwino, inetu ndili pafupi kufa. Kodi ukulu wangawo udzandipinduliranji?” Yakobe adati, “Uyambe walumbira kuti ukulu wakowo wandipatsadi.” Apo Esau adalumbira, nagulitsa ukulu wake wauchisamba kwa Yakobe.
Explore Gen. 25:32-33
5
Gen. 25:26
Pobadwa mng'ono wake, dzanja lake linali litagwira chidendene cha Esau. Motero adamutcha Yakobe. Pamene ana ameneŵa ankabadwa, nkuti Isaki ali wa zaka 60.
Explore Gen. 25:26
6
Gen. 25:28
Tsono Isaki ankakonda Esau chifukwa ankadya nyama imene Esauyo ankamupatsa akapha. Koma Rebeka ankakonda Yakobe.
Explore Gen. 25:28
Home
Bible
Plans
Videos