1
MATEYU 26:41
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Chezerani ndi kupemphera, kuti mungalowe m'kuyesedwa: mzimutu uli wakufuna, koma thupi lili lolefuka.
Compare
Explore MATEYU 26:41
2
MATEYU 26:38
Pamenepo ananena kwa iwo, Moyo wanga uli wozingidwa ndi chisoni cha kufika nacho kuimfa; khalani pano muchezere pamodzi ndi Ine.
Explore MATEYU 26:38
3
MATEYU 26:39
Ndipo anamuka patsogolo pang'ono, nagwa nkhope yake pansi, napemphera, nati, Atate ngati nkutheka, chikho ichi chindipitirire Ine; koma si monga ndifuna Ine, koma Inu.
Explore MATEYU 26:39
4
MATEYU 26:28
pakuti ichi ndi mwazi wanga wa pangano wothiridwa chifukwa cha anthu ambiri ku kuchotsa machimo.
Explore MATEYU 26:28
5
MATEYU 26:26
Ndipo pamene iwo analinkudya, Yesu anatenga mkate, nadalitsa, naunyema; ndipo m'mene anapatsa kwa ophunzira, anati, Tengani, idyani; ichi ndi thupi langa.
Explore MATEYU 26:26
6
MATEYU 26:27
Ndipo pamene anatenga chikho, anayamika, napatsa iwo, nanena, Mumwere ichi inu nonse
Explore MATEYU 26:27
7
MATEYU 26:40
Ndipo anadza kwa ophunzira, nawapeza iwo ali m'tulo, nanena kwa Petro, Nkutero kodi? Simukhoza kuchezera ndi Ine mphindi imodzi?
Explore MATEYU 26:40
8
MATEYU 26:29
Ndipo ndinena kwa inu, sindidzamwanso chipatso ichi champesa, kufikira tsiku limene ndidzamwa chatsopano, pamodzi ndi inu, mu Ufumu wa Atate wanga.
Explore MATEYU 26:29
9
MATEYU 26:75
Ndipo Petro anakumbukira mau amene Yesu adati, Asanalire tambala udzandikana katatu. Ndipo anatulukira kunja, nalira ndi kuwawa mtima.
Explore MATEYU 26:75
10
MATEYU 26:46
Ukani, timuke; taonani, iye wakundipereka wayandikira.
Explore MATEYU 26:46
11
MATEYU 26:52
Pomwepo Yesu ananena kwa iye, Tabweza lupanga lako m'chimakemo, pakuti onse akugwira lupanga adzaonongeka ndi lupanga.
Explore MATEYU 26:52
Home
Bible
Plans
Videos