1
YEREMIYA 50:34
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Mombolo wao ngwa mphamvu; dzina lake Yehova wa makamu: adzawanenera mlandu wao ndithu; kuti apumutse dziko lapansi, nadzidzimutse okhala m'Babiloni.
Compare
Explore YEREMIYA 50:34
2
YEREMIYA 50:6
Anthu anga anakhala nkhosa zotayika; abusa ao anazisokeretsa pa mapiri onyenga; achoka kuphiri kunka kuchitunda; aiwala malo ao akupuma.
Explore YEREMIYA 50:6
3
YEREMIYA 50:20
Masiku omwewo, nthawi yomweyo, ati Yehova, zoipa za Israele zidzafunidwa, koma zidzasoweka; ndi zochimwa za Yuda, koma sizidzapezeka; pakuti ndidzakhululukira iwo amene ndidzawasiya ngati chotsala.
Explore YEREMIYA 50:20
Home
Bible
Plans
Videos