1
YEREMIYA 2:13
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Pakuti anthu anga anachita zoipa ziwiri; anandisiya Ine kasupe wa madzi amoyo, nadziboolera zitsime, zitsime zong'aluka, zosakhalamo madzi.
Compare
Explore YEREMIYA 2:13
2
YEREMIYA 2:19
Choipa chako dzidzakulanga iwe, mabwerero ako adzakudzudzula iwe; dziwa, nuone, kuti ichi ndi choipa ndi chowawa, kuti wasiya Yehova Mulungu wako, ndi kuti kundiopa Ine sikuli mwa iwe, ati Yehova Mulungu wa makamu.
Explore YEREMIYA 2:19
3
YEREMIYA 2:11
Kodi mtundu wa anthu unasintha milungu yao, imene siili milungu? Koma anthu anga anasintha ulemerero wao ndi chosapindula.
Explore YEREMIYA 2:11
Home
Bible
Plans
Videos