1
YEREMIYA 13:23
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Kodi angathe Mkusi kusanduliza khungu lake, kapena nyalugwe mawanga ake? Pamenepo mungathe inunso kuchita zabwino, inu amene muzolowera kuchita zoipa.
Compare
Explore YEREMIYA 13:23
2
YEREMIYA 13:16
Lemekezani Yehova Mulungu wanu, kusanade, mapazi anu asanakhumudwe pa mapiri achizirezire; nimusanayembekeze kuunika, Iye asanasandutse kuunikaku mthunzi wa imfa, ndi kukuyesa mdima wa bii.
Explore YEREMIYA 13:16
3
YEREMIYA 13:10
Anthu oipa awa, amene akana kumva mau anga, amene ayenda m'kuumirira kwa mtima wao, atsata milungu ina kuitumikira, ndi kuigwadira, adzakhala ngati mpango uwu, wosayenera kanthu.
Explore YEREMIYA 13:10
4
YEREMIYA 13:15
Tamvani inu, Tcherani khutu; musanyade, pakuti Yehova wanena.
Explore YEREMIYA 13:15
Home
Bible
Plans
Videos