1
EKSODO 25:8-9
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndipo andimangire malo opatulika; kuti ndikhale pakati pao. Monga mwa zonse Ine ndilikuonetsa iwe, chifaniziro cha Kachisi, ndi chifaniziro cha zipangizo zake zonse, momwemo uchimange.
Compare
Explore EKSODO 25:8-9
2
EKSODO 25:2
Lankhula ndi ana a Israele, kuti anditengere chopereka; ulandire chopereka changa kwa munthu aliyense mtima wake umfunitsa mwini.
Explore EKSODO 25:2
Home
Bible
Plans
Videos