1
DEUTERONOMO 23:23
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Chotuluka pa milomo yanu muchisamalire ndi kuchichita; monga munalonjezera Yehova Mulungu wanu, chopereka chaufulu munachilonjeza pakamwa panu.
Compare
Explore DEUTERONOMO 23:23
2
DEUTERONOMO 23:21
Mukawindira Yehova Mulungu wanu chowinda, musamachedwa kuchichita; popeza Yehova Mulungu wanu adzakufunsani za ichi ndithu ndipo mukadachimwako.
Explore DEUTERONOMO 23:21
3
DEUTERONOMO 23:22
Koma mukapanda kulonjeza chowinda, mulibe kuchimwa.
Explore DEUTERONOMO 23:22
Home
Bible
Plans
Videos