1
2 YOHANE 1:6
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndipo chikondi ndi ichi, kuti tiyende monga mwa malamulo ake. Ili ndi lamulolo, monga mudalimva kuyambira pachiyambi, kuti mukayende momwemo.
Compare
Explore 2 YOHANE 1:6
2
2 YOHANE 1:9
Yense wakupitirira, wosakhala m'chiphunzitso cha Khristu, alibe Mulungu; iye wakukhala m'chiphunzitso, iyeyo ali nao Atate ndi Mwana.
Explore 2 YOHANE 1:9
3
2 YOHANE 1:8
Mudzipenyerere nokha, kuti mungataye zimene tazichita, koma kuti mulandire mphotho yokwanira.
Explore 2 YOHANE 1:8
4
2 YOHANE 1:7
Pakuti onyenga ambiri adatuluka kulowa m'dziko lapansi, ndiwo amene savomereza kuti Yesu Khristu anadza m'thupi. Ameneyo ndiye wonyenga ndi wokana Khristu.
Explore 2 YOHANE 1:7
Home
Bible
Plans
Videos