1
1 YOHANE 1:9
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ngati tivomereza machimo athu, ali wokhulupirika ndi wolungama Iye, kuti atikhululukire machimo athu, ndi kutisambitsa kutichotsera chosalungama chilichonse.
Compare
Explore 1 YOHANE 1:9
2
1 YOHANE 1:7
koma ngati tiyenda m'kuunika, monga Iye ali m'kuunika, tiyanjana wina ndi mnzake, ndipo mwazi wa Yesu Mwana wake utisambitsa kutichotsera uchimo wonse.
Explore 1 YOHANE 1:7
3
1 YOHANE 1:8
Tikati kuti tilibe uchimo, tidzinyenga tokha, ndipo mwa ife mulibe choonadi.
Explore 1 YOHANE 1:8
4
1 YOHANE 1:5-6
Ndipo uwu ndi uthenga tidaumva kwa Iye, ndipo tiulalikira kwa inu, kuti Mulungu ndiye kuunika, ndipo mwa Iye monse mulibe mdima. Tikati kuti tiyanjana ndi Iye, ndipo tiyenda mumdima, tinama, ndipo sitichita choonadi
Explore 1 YOHANE 1:5-6
5
1 YOHANE 1:10
Tikanena kuti sitidachimwa, timuyesa Iye wonama, ndipo mau ake sakhala mwa ife.
Explore 1 YOHANE 1:10
Home
Bible
Plans
Videos