1
Masalimo 102:2
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Musandibisire nkhope yanu pamene ndili pa msautso. Munditcherere khutu; pamene ndiyitana ndiyankheni msanga.
Compare
Explore Masalimo 102:2
2
Masalimo 102:1
Yehova imvani pemphero langa; kulira kwanga kopempha thandizo kufike kwa Inu.
Explore Masalimo 102:1
3
Masalimo 102:12
Koma Inu Yehova, muli pa mpando wanu waufumu kwamuyaya; kudziwika kwanu ndi kokhazikika ku mibado yonse.
Explore Masalimo 102:12
4
Masalimo 102:17
Iye adzayankha pemphero la anthu otayika; sadzanyoza kupempha kwawo.
Explore Masalimo 102:17
Home
Bible
Plans
Videos