1
Masalimo 101:3
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Sindidzayika chinthu chilichonse choyipa pamaso panga. Ine ndimadana ndi zochita za anthu opanda chikhulupiriro; iwo sadzadziphatika kwa ine.
Compare
Explore Masalimo 101:3
2
Masalimo 101:2
Ndidzatsata njira yolungama; nanga mudzabwera liti kwa ine? Ndidzayenda mʼnyumba mwanga ndi mtima wosalakwa.
Explore Masalimo 101:2
3
Masalimo 101:6
Maso anga adzakhala pa okhulupirika mʼdziko, kuti akhale pamodzi ndi ine; iye amene mayendedwe ake ndi wosalakwa adzanditumikira.
Explore Masalimo 101:6
Home
Bible
Plans
Videos