1
2 Akorinto 13:5
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Tadzisanthulani nokha kuti muone ngati muli mʼchikhulupiriro; dziyeseni nokha. Kodi simuzindikira kuti Khristu Yesu ali mwa inu, ngati si choncho mwalephera mayesowa?
Compare
Explore 2 Akorinto 13:5
2
2 Akorinto 13:14
Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu, ndi chikondi cha Mulungu, ndi chiyanjano cha Mzimu Woyera zikhale ndi inu nonse.
Explore 2 Akorinto 13:14
3
2 Akorinto 13:11
Potsiriza abale, ndikuti tsalani bwino. Yesetsani kukhala angwiro, mvetsetsani pempho langa, khalani a mtima umodzi, khalani mwamtendere. Ndipo Mulungu wachikondi ndi mtendere adzakhala nanu.
Explore 2 Akorinto 13:11
Home
Bible
Plans
Videos