1
ZEKARIYA 5:3
Buku Lopatulika
Ndipo anati kwa ine, Ili ndi temberero lilikutulukira padziko lonse; pakuti aliyense wakuba adzapirikitsidwa kuno monga mwa ili; ndi aliyense wakulumbira zonama adzapirikitsidwa kuno monga mwa ili.
Compare
Explore ZEKARIYA 5:3
Home
Bible
Plans
Videos