1
ZEKARIYA 1:3
Buku Lopatulika
Chifukwa chake uziti nao, Atero Yehova wa makamu: Bwererani kudza kwa Ine, ati Yehova wa makamu, ndipo Ine ndidzabwerera kudza kwa inu, ati Yehova wa makamu.
Compare
Explore ZEKARIYA 1:3
2
ZEKARIYA 1:17
Fuulanso, ndi kuti, Atero Yehova wa makamu: Mizinda yanga idzalemerera ndi kufalikiranso; ndipo Yehova adzasangalatsanso Ziyoni, nadzasankhamo Yerusalemu.
Explore ZEKARIYA 1:17
Home
Bible
Plans
Videos