Zitatha izi Mulungu anati, “Tipange munthu mʼchifanizo chathu, mofanana ndi ife kuti alamulire nsomba za mʼnyanja, mbalame zamlengalenga, nyama zonse zoweta ndi zonse zokwawa za pa dziko lapansi ndi zamoyo zonse zakutchire.” Ndipo Mulungu analenga munthu mʼchifanizo chake. Anawalengadi mʼchifanizo cha Mulungu; analenga iwo, mwamuna ndi mkazi.
إقرأ Genesis 1
استمع إلى Genesis 1
شارك
قارن كل الترجمات: Genesis 1:26-27
احفظ الآيات، اقرأ دون الاتصال بالإنترنت، شاهد فيديوهات تعليمية، والمزيد!
تستخدم YouVersion ملفات تعريف الإرتباط لتخصيص تجربتك. بإستخدامك لموقعنا الإلكتروني، فإنك تقبل إستخدامنا لملفات تعريف الإرتباط كما هو موضح في سياسة الخصوصية
الصفحة الرئيسية
الكتاب المقدس
خطط
فيديوهات