1
Genesis 44:34
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Ndingabwerere bwanji kwa abambo anga ngati sindingapite ndi mnyamatayu? Ayi! Sindifuna kukaona tsoka limene lingakagwere abambo anga.”
አወዳድር
{{ጥቅስ}} ያስሱ
2
Genesis 44:1
Pambuyo pake Yosefe analamulira wantchito wa mʼnyumba mwake kuti, “Adzazire chakudya anthuwa mʼmatumba mwawo monga mmene anganyamulire, ndipo uwayikire ndalama zawo pakamwa pa matumba awowo.
ቤት
መጽሐፍ ቅዱስ
እቅዶች
ቪዲዮዎች