1
Genesis 43:23
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Koma iye anati, “Mitima yanu ikhale pansi ndipo musachite mantha. Mulungu wanu, Mulungu wa abambo anu, anakuyikirani chumacho mʼmatumba anu. Ine ndinalandira ndalama zanu.” Ndipo anakawatulutsira Simeoni.
አወዳድር
{{ጥቅስ}} ያስሱ
2
Genesis 43:30
Kenaka Yosefe anafulumira kutuluka chifukwa mtima wake unadzaza ndi chifundo cha mngʼono wake ndipo anafuna kulira. Tsono anakalowa mʼchipinda chakechake nakalira kumeneko.
ቤት
መጽሐፍ ቅዱስ
እቅዶች
ቪዲዮዎች