1
Eksodo 1:17
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Koma azambawo ankaopa Mulungu ndipo sanachite zimene mfumu ya Igupto inawawuza kuti achite. Iwo analeka ana aamuna kuti akhale ndi moyo.
አወዳድር
{{ጥቅስ}} ያስሱ
2
Eksodo 1:12
Koma pamene ankawazunza kwambiri, Aisraeli ndiye ankachulukirachulukira mpaka kubalalikira mʼdziko lonse. Kotero Aigupto anayamba kuopa Aisraeliwo
3
Eksodo 1:21
Pakuti azambawo ankaopa Mulungu, Iye anawapatsa mabanja awoawo.
4
Eksodo 1:8
Pambuyo pake mfumu yatsopano imene sinkamudziwa Yosefe, inayamba kulamulira dziko la Igupto.
ቤት
መጽሐፍ ቅዱስ
እቅዶች
ቪዲዮዎች