GENESIS 6:7

GENESIS 6:7 BLPB2014

Ndipo anati Yehova, Ndidzafafaniza anthu amene ndawalenga pa dziko lapansi; anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga: pakuti ndimva chisoni chifukwa ndapanga izo.

Video vir GENESIS 6:7

Gratis leesplanne en oordenkings oor GENESIS 6:7