LUKA 14:34-35

LUKA 14:34-35 BLP-2018

Kotero mchere uli wokoma; koma ngati mchere utasukuluka adzaukoleretsa ndi chiyani? Suyenera kuuthira pamunda kapena padzala, autaya kunja. Amene ali nao makutu akumva amve.

Ividiyo ye- LUKA 14:34-35