1
YOHANE 9:4
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Tiyenera kugwira ntchito za Iye wondituma Ine, pokhala pali msana; ukudza usiku pamene palibe munthu angakhoze kugwira ntchito.
对照
探索 YOHANE 9:4
2
YOHANE 9:5
Pakukhala Ine m'dziko lapansi, ndili kuunika kwa dziko lapansi.
探索 YOHANE 9:5
3
YOHANE 9:2-3
Ndipo ophunzira ake anamfunsa Iye, nanena, Rabi, anachimwa ndani, ameneyo, kapena atate wake ndi amake, kuti anabadwa wosaona? Yesu anayankha, Sanachimwe ameneyo, kapena atate wake ndi amake; koma kuti ntchito za Mulungu zikaonetsedwe mwa iye.
探索 YOHANE 9:2-3
4
YOHANE 9:39
Ndipo Yesu anati, Kudzaweruza ndadza Ine kudziko lino lapansi, kuti iwo osapenya apenye; ndi kuti iwo akupenya akhale osaona.
探索 YOHANE 9:39
主页
圣经
计划
视频