YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

YOHANE 7 的热门经文

1

YOHANE 7:38

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Iye wokhulupirira Ine, monga chilembo chinati, Mitsinje ya madzi amoyo idzayenda, kutuluka m'kati mwake.

对照

探索 YOHANE 7:38

2

YOHANE 7:37

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma tsiku lomaliza, lalikululo la chikondwerero, Yesu anaimirira nafuula, ndi kunena, Ngati pali munthu akumva ludzu, adze kwa Ine, namwe.

对照

探索 YOHANE 7:37

3

YOHANE 7:39

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma ichi anati za Mzimu, amene iwo akukhulupirira Iye anati adzalandire; pakuti Mzimu panalibe pamenepo, chifukwa Yesu sanalemekezedwe panthawi pomwepo.

对照

探索 YOHANE 7:39

4

YOHANE 7:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Musaweruze monga maonekedwe, koma weruzani chiweruziro cholungama.

对照

探索 YOHANE 7:24

5

YOHANE 7:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Iye wolankhula zochokera kwa iye yekha afuna ulemu wa mwini yekha. Iye wakufuna ulemu wa Iye amene anamtuma, yemweyu ali woona, ndipo mwa Iye mulibe chosalungama.

对照

探索 YOHANE 7:18

6

YOHANE 7:16

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pamenepo Yesu anayankha iwo, nati, Chiphunzitso changa sichili changa, koma cha Iye amene anandituma Ine.

对照

探索 YOHANE 7:16

7

YOHANE 7:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Dziko lapansi silingathe kudana ndi inu; koma Ine lindida popeza Ine ndilichitira umboni, kuti ntchito zake zili zoipa.

对照

探索 YOHANE 7:7

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频