1
Yohane 3:16
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
“Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha.
Karşılaştır
Yohane 3:16 keşfedin
2
Yohane 3:17
Pakuti Mulungu sanatume Mwana wake ku dziko lapansi, kuti akaweruze, koma kuti akapulumutse dziko lapansi.
Yohane 3:17 keşfedin
3
Yohane 3:3
Poyankha Yesu ananena kuti, “Zoonadi, Ine ndikukuwuza kuti, ngati munthu sabadwanso mwatsopano sangathe kuona ufumu wa Mulungu.”
Yohane 3:3 keşfedin
4
Yohane 3:18
Aliyense wokhulupirira Iye saweruzidwa, koma aliyense wosakhulupirira waweruzidwa kale chifukwa sanakhulupirire dzina la Mwana wobadwa yekha wa Mulungu.
Yohane 3:18 keşfedin
5
Yohane 3:19
Ndipo chiweruzo ndi ichi: kuwunika kunabwera mʼdziko lapansi, koma anthu anakonda mdima mʼmalo mwa kuwunikako, chifukwa ntchito zawo zinali zoyipa.
Yohane 3:19 keşfedin
6
Yohane 3:30
Nʼkoyenera kuti Iyeyo akule, ine ndichepe.
Yohane 3:30 keşfedin
7
Yohane 3:20
Aliyense wochita zoyipa amadana ndi kuwunika, ndipo sabwera poyera chifukwa cha mantha kuti ntchito zake zingaonekere.
Yohane 3:20 keşfedin
8
Yohane 3:36
Aliyense wokhulupirira Mwanayo ali ndi moyo wosatha, koma iye amene samvera Mwanayo sadzawuona moyo, pakuti mkwiyo wa Mulungu umakhala pa iye.”
Yohane 3:36 keşfedin
9
Yohane 3:14
Tsono monga Mose anapachika njoka mʼchipululu, moteronso Mwana wa Munthu ayenera kupachikidwa
Yohane 3:14 keşfedin
10
Yohane 3:35
Atate amakonda Mwana ndipo apereka zonse mʼmanja mwake.
Yohane 3:35 keşfedin
Ana Sayfa
Kutsal Kitap
Okuma Planları
Videolar