1
Yohane 18:36
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Yesu anati, “Ufumu wanga si wa dziko lapansi lino. Ukanakhala wa pansi pano, antchito anga akanachita nkhondo kulepheretsa Ayuda kundigwira. Koma tsopano ufumu wanga ndi wochokera kumalo ena.”
Karşılaştır
Yohane 18:36 keşfedin
2
Yohane 18:11
Yesu analamula Petro kuti, “Bwezera lupanga mʼchimake! Kodi Ine ndisamwere chikho chimene Atate andipatsa?”
Yohane 18:11 keşfedin
Ana Sayfa
Kutsal Kitap
Okuma Planları
Videolar