Logo ng YouVersion
Hanapin ang Icon

Lk. 8:15

Lk. 8:15 BLY-DC

Koma mbeu zogwera pa nthaka yabwino zija zikutanthauza anthu amene amaŵamva mau a Mulungu, naŵasunga mu mtima woona ndi wabwino, ndipo amalimbikira mpaka kubereka zipatso.”