Logo ng YouVersion
Hanapin ang Icon

Lk. 8:12

Lk. 8:12 BLY-DC

Mbeu zogwera m'njira zija zikutanthauza anthu amene amaŵamva mau a Mulungu. Koma Satana amabwera, nkuchotsa mau aja m'mitima mwao, kuwopa kuti angakhulupirire ndi kupulumuka.