Ntc. 24:25
Ntc. 24:25 BLY-DC
Koma pamene Paulo adakamba za chilungamo, za kudziletsa, ndi zakuti Mulungu adzaweruza anthu, Felikisi adachita mantha namuuza kuti, “Pakali pano bapita, ndikapeza nthaŵi, ndichita kukuitananso.”
Koma pamene Paulo adakamba za chilungamo, za kudziletsa, ndi zakuti Mulungu adzaweruza anthu, Felikisi adachita mantha namuuza kuti, “Pakali pano bapita, ndikapeza nthaŵi, ndichita kukuitananso.”