Logo ng YouVersion
Hanapin ang Icon

Ntc. 23:11

Ntc. 23:11 BLY-DC

Tsiku lomwelo, usiku, Ambuye adadzaima pafupi ndi Paulo namuuza kuti, “Limba mtima. Monga wandichitira umboni kuno ku Yerusalemu, uyenera kukandichitiranso umboni ku Roma.”