1
Lk. 19:10
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Pajatu Mwana wa Munthu adabwera kudzafunafuna ndi kudzapulumutsa amene adatayika.”
Paghambingin
I-explore Lk. 19:10
2
Lk. 19:38
Adati, “Ndi yodala Mfumu imene ilikudza m'dzina la Ambuye. Mtendere Kumwamba, ulemu kwa Mulungu kumwambamwamba.”
I-explore Lk. 19:38
3
Lk. 19:9
Apo Yesu adamuuza kuti, “Chipulumutso chafika m'banja lino lero, popeza kuti ameneyunso ndi mwana wa Abrahamu.
I-explore Lk. 19:9
4
Lk. 19:5-6
Ndiye pamene Yesu adafika pamalopo, adayang'ana m'mwamba, namuuza kuti, “Zakeyo, fulumira, tsika, chifukwa lero ndikuyenera kukakhala nao kunyumba kwako.” Pompo Zakeyo adafulumira, natsika, kenaka nkukamlandiradi Yesu mokondwa kwambiri.
I-explore Lk. 19:5-6
5
Lk. 19:8
Koma Zakeyo adaimirira nauza Ambuye kuti, “Ambuye, ndithudi ndidzapereka hafu la chuma changa kwa amphaŵi. Ndipo ngati ndidalandira kanthu kwa munthu aliyense monyenga, ndidzamubwezera kanai.”
I-explore Lk. 19:8
6
Lk. 19:39-40
Apo Afarisi ena amene adaali m'khamumo adauza Yesu kuti, “Aphunzitsi, auzeni ophunzira anuŵa aleke zimenezi.” Iye adati, “Ndikutitu iwoŵa akangokhala chete, ifuula ndi miyalayi.”
I-explore Lk. 19:39-40
Home
Biblia
Mga Gabay
Mga Palabas