1
Lk. 11:13
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Tsono ngati inu, nkuipa kwanuku, mumadziŵa kupatsa ana anu mphatso zabwino, nanji Atate akumwamba, angalephere bwanji kupereka Mzimu Woyera kwa amene aŵapempha.”
Paghambingin
I-explore Lk. 11:13
2
Lk. 11:9
“Motero ndikukuuzani kuti, Pemphani ndipo adzakupatsani. Funafunani ndipo mudzapeza. Gogodani, ndipo adzakutsekulirani.
I-explore Lk. 11:9
3
Lk. 11:10
Paja munthu amene amapempha, ndiye amalandira, amene amafunafuna, ndiye amapeza, ndipo amene amagogoda, ndiye amamtsekulira.
I-explore Lk. 11:10
4
Lk. 11:2
Yesu adati, “Pamene mukupemphera muziti, “ ‘Atate, dzina lanu lilemekezedwe. Ufumu wanu udze.
I-explore Lk. 11:2
5
Lk. 11:4
Mutikhululukire ife machimo athu, pakuti ifenso timakhululukira aliyense wotilakwira. Ndipo musalole kuti tigwe m'zotiyesa.’ ”
I-explore Lk. 11:4
6
Lk. 11:3
Mutipatse ife tsiku lililonse chakudya chathu chamasikuwonse.
I-explore Lk. 11:3
7
Lk. 11:34
Maso ndiwo nyale zounikira thupi lako. Ngati maso ako ali bwino, m'thupi mwako monse mumakhala kuŵala. Koma ngati maso ako sali bwino, m'thupi mwako monse mumakhala mdima.
I-explore Lk. 11:34
8
Lk. 11:33
“Munthu sati akayatsa nyale, nkuiika m'chipinda chapansi kapena kuivundikira ndi mbiya. Koma amaiika pa malo oonekera, kuti anthu oloŵa m'nyumbamo aone kuŵala kwake.
I-explore Lk. 11:33
Home
Biblia
Mga Gabay
Mga Palabas