Gen. 35:1
Gen. 35:1 BLY-DC
Tsono Mulungu adauza Yakobe kuti, “Nyamuka, pita ku Betele, ukakhale komweko. Ukamangeko guwa la Mulungu amene adakuwonekera pamene unkathaŵa mbale wako Esau.”
Tsono Mulungu adauza Yakobe kuti, “Nyamuka, pita ku Betele, ukakhale komweko. Ukamangeko guwa la Mulungu amene adakuwonekera pamene unkathaŵa mbale wako Esau.”