1
Gen. 10:8
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Kusi adabereka Nimirodi. Nimirodi anali wankhondo woyamba wanyonga pa dziko lapansi.
เปรียบเทียบ
สำรวจ Gen. 10:8
2
Gen. 10:9
Iyeyu analinso mlenje wamkulu pamaso pa Chauta. Nchifukwa chake anthu ali ndi chisudzo chakuti, “Ndiwe mlenje wamkulu pamaso pa Chauta, ngati Nimirodi.”
สำรวจ Gen. 10:9
หน้าหลัก
พระคัมภีร์
แผนการอ่านต่างๆ
วิดีโอ