1
Genesis 7:1
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Ndipo Yehova anati kwa Nowa, “Lowa mu chombo iwe ndi banja lako lonse, chifukwa ndaona kuti ndiwe wolungama mu mʼbado uwu.
ஒப்பீடு
Genesis 7:1 ஆராயுங்கள்
2
Genesis 7:24
Madziwo anadzaza dziko lonse lapansi kwa masiku 150.
Genesis 7:24 ஆராயுங்கள்
3
Genesis 7:11
Pa tsiku la 17 la mwezi wachiwiri, Nowa ali ndi zaka 600, akasupe onse akuya kwambiri anasefuka ndiponso zitseko za madzi akumwamba zinatsekuka.
Genesis 7:11 ஆராயுங்கள்
4
Genesis 7:23
Chamoyo chilichonse pa dziko lapansi chinawonongedwa, kuyambira munthu, nyama, zokwawa ndi mbalame. Nowa yekha ndiye anatsala pamodzi ndi onse amene anali naye.
Genesis 7:23 ஆராயுங்கள்
5
Genesis 7:12
Ndipo mvula inagwa pa dziko lapansi masiku makumi anayi usana ndi usiku.
Genesis 7:12 ஆராயுங்கள்
முகப்பு
வேதாகமம்
வாசிப்புத் திட்டங்கள்
காணொளிகள்