YouVersion logo
Dugme za pretraživanje

Yoh. 1:10-11

Yoh. 1:10-11 BLY-DC

Wotchedwa Mauyo anali m'dziko lapansi, ndipo Mulungu adalenga dziko lapansilo kudzera mwa Iye, komabe anthu apansipano sadamzindikire. Adaabwera kwao ndithu, koma anthu ake omwe sadamlandire.